?? ?? ??Nyanja الشيشوا Chichewa, Chinyanja

85 قناة ياو ملاوي Yao language – Yankee Champion

YouTube

https://youtube.com/playlist?list=PLBFEt29we81QdL2wFg8aAoa41-MuttduC

facebook
https://www.facebook.com/85-%D9%82%D9%86%D8%A7%D8%A9-%D9%8A%D8%A7%D9%88-%D9%85%D9%84%D8%A7%D9%88%D9%8A-Yao-language-Yankee-Champion-105242765449169/

Telegram
https://t.me/sarhan006

?https://sarhaan.com/a/%d9%8a%d8%a7%d9%88-%d9%85%d9%84%d8%a7%d9%88%d9%8a/

مناطق التحدث بها:ملاوي، والبلاد المجاورة كجنوب إفريقيا، وموزنبيق

عدد الناطقين بها: نحو ٥ مليون

ZISONYEZO ZA UTUMIKI (CHICHEWA)

Share this book                 (دلائل النبوَّة) و(أعلام النبوَّة) القرآن الكريم تشيشوا ZISONYEZO ZA UTUMIKI (CHICHEWA) QURAN YOLEMEKEZEKA: Adayankhula Yahyah bin Aktham kunena kuti: Māmuun yemwe adali mtsogoleri wa asilamu nthawi imeneyo,adachititsa mkumano wa mtsutso (debate), ndiye kunalowa muyuda wina mchigulu cha anthu omwe anafika ku mtsutso kuja, muyudayu anali atavala bwino, nkhope ikuoneka bwino komanso amamveka kafungo […]

ZISONYEZO ZA UTUMIKI (CHICHEWA) Read More »

MITUNDU YA TAUHEED

Share this book                 Kumupatula Allah (olemekezeka) muzinthuzimene wapatulika nazo, kumbali yaumbuye,umulungu ndi maina komanso mbirizake. إفراد الله (عز وجل) بما يختص به من الربوبية, والألوهية, والأسماء والصفات NDIPO MITUNDU YAKE ILIPO ITATU: وأنواعه ثلاثة 1-Tauheed ya umbuye(al-rububiyyah): توحيد الربوبية Kumeneko ndiko kumupatula Allah pa zintchito zake, kapena kumupatula Allah pa kulenga,umwini pa chilichonse ndikuyendetsa zinthu. هو

MITUNDU YA TAUHEED Read More »

MLONDORI WA ONGOLOWA KUMENE CHISILAMU, KAPENA KUTI; CHISILAMU NDI CHIYANI?

Share this book                 MLONDORI WA ONGOLOWA KUMENE CHISILAMU, KAPENA KUTI; CHISILAMU NDI CHIYANI? MASAMBA OWONGOLERA KUCHIDZIWA CHIPEMBEDZO CHA CHISILAMU, NDIKUMPHUNZITSA MSILAMU ZITHU ZOFUNIKA PA CHIPEMBEDZO. WOLEMBA NDI; SHEIKH HAITHAM SARHAN (ALLAH AWASAMALIRE). MMENEMU MULI: 1: TSAMBA LOFOTOKOZA ZA TAUHEED (UMODZI WA ALLA) PAMODZI NDI MITUNDU YAKE, KOMANSO MAGAWO AKULU A CHIPEMBEDZO, NDI MITUNDU YA ZOLETSEDWA. 2:

MLONDORI WA ONGOLOWA KUMENE CHISILAMU, KAPENA KUTI; CHISILAMU NDI CHIYANI? Read More »

NDINGALOWE BWANJI CHISILAMU?

Share this book                 Kodi kulowa chisilamu ndikophweka? ٍ Eya kulowa chisilamu ndikophweka chifukwa sizimasaukila mkhala pakati. Kodi ndikuyenera kuchita changu kulowa chisilamu? kapena ndikuyenera kudikila nthawi yoyenera? kapena ndikuyenera kuthetsa kaye ena mwa mavuto? Ndizoyenera kuchita changu kulowa chisilamu, chifukwa kuchedwetsa kulowa chisilamu kukhoza kubweresa chionongeko, utha kumwalira nthawi iliyonse, ngati mmene zilili kuti kulowa chisilamu

NDINGALOWE BWANJI CHISILAMU? Read More »

SWAUM(KUSALA) ILI MMAGULU AWIRI

Share this book                  SWAUM(KUSALA) ILI MMAGULU AWIRI: الصيام قسمان YOKAKAMIZIKA (WAJIBU): Iyi ndi yomwe imachitika mmwezi wa Ramadhani, ina ndi ya Dipo(kaffarah) ndi ya Lonjezo(nadhir). واجب : في رمضان و الكفارات و النذور YA SUNNAH: Iyi ndi yomwe imachitika posakhala nthawi zitatuzi. نفل : في غير ذلك TANTHAUZO LA SWAUM(KUSALA):     تعريف الصيام Uku

SWAUM(KUSALA) ILI MMAGULU AWIRI Read More »

SWAUM(KUSALA) ILI MMAGULU AWIRI

Share this book                 الزكاة CHICHEWA اللغة العربية ZAKATI ILI MMAGULU AWIRI الـزكاة قـسـمان: YA SUNNAH: Ndipo ichi ndi chuma chilichonse chimene munthu amapeleka mu njira ya ibadah(kumpembedza Mulungu). نافلة : و هي كل مال يخرجه الإنسان على وجه التعبد المحض . YA FARADH (YOKAKAMIZIKA) فريضة : Iyi ili mmagulu awiri:  🙁 وهي نوعان ) ZAKATI YA

SWAUM(KUSALA) ILI MMAGULU AWIRI Read More »

QUR’AN YOLEMEKEZEKA yotanthauzidwa m’chichewa

Share this book                  QUR’AN YOLEMEKEZEKA yotanthauzidwa m’chichewa Chifukwa chakufunika kwa uthengawu kuti ufike kwa anthu onse, a Bungwe la Africa Muslim Agency adandipempha kuti ndimasulire Qur’an m’chichewa, ndicholinga chakuti amene sangathe kumvetsa uthenga wake m’chiarabu, aumve m’chilankhulo chawo cha Chichewa. Choncho ntchitoyi idagwirikadi kotero kuti munthu akawerenga bwinobwino akhoza kumva uthenga wa Mulungu m’Qur’an. Ndayetsetsa

QUR’AN YOLEMEKEZEKA yotanthauzidwa m’chichewa Read More »

Scroll to Top