ZISONYEZO ZA UTUMIKI (CHICHEWA)
Share this book (دلائل النبوَّة) و(أعلام النبوَّة) القرآن الكريم تشيشوا ZISONYEZO ZA UTUMIKI (CHICHEWA) QURAN YOLEMEKEZEKA: Adayankhula Yahyah bin Aktham kunena kuti: Māmuun yemwe adali mtsogoleri wa asilamu nthawi imeneyo,adachititsa mkumano wa mtsutso (debate), ndiye kunalowa muyuda wina mchigulu cha anthu omwe anafika ku mtsutso kuja, muyudayu anali atavala bwino, nkhope ikuoneka bwino komanso amamveka kafungo […]
ZISONYEZO ZA UTUMIKI (CHICHEWA) Read More »